Mateyu 26:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo anabweranso, nawapeza iwo ali m'tulo, pakuti zikope zao zinalemera ndi tulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo anabweranso, nawapeza iwo ali m'tulo, pakuti zikope zao zinalemera ndi tulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Pamene adabwerakonso, adaŵapeza ali m'tulo, chifukwa zikope zao zinkalemera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Atabweranso anawapeza ali mtulo chifukwa zikope zawo zinalemedwa ndi tulo. Onani mutuwo |