Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 26:43 - Buku Lopatulika

43 Ndipo anabweranso, nawapeza iwo ali m'tulo, pakuti zikope zao zinalemera ndi tulo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 Ndipo anabweranso, nawapeza iwo ali m'tulo, pakuti zikope zao zinalemera ndi tulo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Pamene adabwerakonso, adaŵapeza ali m'tulo, chifukwa zikope zao zinkalemera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Atabweranso anawapeza ali mtulo chifukwa zikope zawo zinalemedwa ndi tulo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 26:43
8 Mawu Ofanana  

Udzafanana ndi wina wogona pakati pa nyanja, pena wogona pansonga ya mlongoti wa ngalawa.


Ndipo mwini chombo anadza kwa iye, nanena naye, Utani iwe wam'tulo? Uka, itana Mulungu wako, kapena Mulunguyo adzatikumbukira tingatayike.


Anamukanso kachiwiri, napemphera, nati, Atate wanga, ngati ichi sichingandipitirire, koma ndimwere ichi, kufuna kwanu kuchitidwe.


Ndipo anawasiyanso, napemphera kachitatu, nateronso mau omwewo.


Koma Petro ndi iwo anali naye analemedwa ndi tulo; koma m'mene anayera m'maso ndithu, anaona ulemerero wake, ndi amuna awiriwo akuimirira ndi Iye.


Ndipo mnyamata dzina lake Yutiko anakhala pazenera, wogwidwa nato tulo tatikulu; ndipo pakukhala chifotokozere Paulo, ndipo pogwidwa nato tulo, anagwa posanja pachiwiri, ndipo anamtola wakufa.


Anthu onse amvere maulamuliro a akulu; pakuti palibe ulamuliro wina koma wochokera kwa Mulungu; ndipo iwo amene alipo aikidwa ndi Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa