Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 26:44 - Buku Lopatulika

44 Ndipo anawasiyanso, napemphera kachitatu, nateronso mau omwewo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 Ndipo anawasiyanso, napemphera kachitatu, nateronso mau omwewo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Yesu adaŵasiyanso, napita kukapemphera kachitatu, akunena mau amodzimodzi omwe aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 Choncho anawasiya napitanso kukapemphera kachitatu nanenanso chimodzimodzi.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 26:44
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anabweranso, nawapeza iwo ali m'tulo, pakuti zikope zao zinalemera ndi tulo.


Pomwepo anadza kwa ophunzira, nanena kwa iwo, Gonani nthawi yatsalayi, mupumule; onani, nthawi yafika, ndipo Mwana wa Munthu aperekedwa m'manja a ochimwa.


Ndipo popemphera musabwerezebwereze chabe iai, monga amachita anthu akunja, chifukwa ayesa kuti adzamvedwa ndi kulankhulalankhula kwao.


Ndipo anawanenera fanizo lakuti ayenera iwo kupemphera nthawi zonse, osafooka mtima;


Za ichi ndinapemphera Ambuye katatu kuti chichoke kwa ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa