Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 12:8 - Buku Lopatulika

8 Za ichi ndinapemphera Ambuye katatu kuti chichoke kwa ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Za ichi ndinapemphera Ambuye katatu kuti chichoke kwa ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Pamenepo ndidapempha Ambuye katatu kuti andichotsere chimenechi,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Katatu konse ndinapempha Ambuye kuti andichotsere.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 12:8
10 Mawu Ofanana  

Ndipo ukatsuka chovalacho, kapena muyaro, kapena mtsendero, kapena chinthu chilichonse chopangika ndi chikopa, ngati nthenda yalekapo pa chimenecho, achitsukenso kawiri, pamenepo chili choyera.


Ndipo ichi chinachitika katatu; ndipo zinakwezekanso zonse kumwamba.


Ndipo momwemonso Mzimu athandiza kufooka kwathu; pakuti chimene tizipempha monga chiyenera, sitidziwa; koma Mzimu mwini atipempherera ndi zobuula zosatheka kuneneka;


Ameneyo, m'masiku a thupi lake anapereka mapemphero ndi mapembedzero pamodzi ndi kulira kwakukulu ndi misozi kwa Iye amene anakhoza kumpulumutsa Iye muimfa, ndipo anamveka popeza anaopa Mulungu,


Kundichititsa chisoni kuti ndinaika Saulo akhale mfumu; pakuti wabwerera wosanditsata Ine, ndipo sanachite malamulo anga. Ndipo Samuele anakwiya; nalira kwa Yehova usiku wonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa