Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:1 - Buku Lopatulika

Ndipo panali pamene Yesu anatha mau onse amenewa, anati kwa ophunzira ake,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali pamene Yesu anatha mau onse amenewa, anati kwa ophunzira ake,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu atatsiriza kulankhula nkhani zonsezi, adauza ophunzira ake kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu atamaliza kuyankhula zonsezi, anati kwa ophunzira ake,

Onani mutuwo



Mateyu 26:1
3 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Yesu anatha mau amenewa, anachokera ku Galileya, nadza ku malire a Yudeya, a ku tsidya lija la Yordani.


Ndipo panakhala pamene Yesu anatha mau amenewa, makamu a anthu anazizwa ndi chiphunzitso chake:


Koma Paska wa Ayuda anali pafupi; ndipo ambiri anakwera kunka ku Yerusalemu kuchoka kuminda, asanafike Paska, kukadziyeretsa iwo okha.