Mateyu 7:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo panakhala pamene Yesu anatha mau amenewa, makamu a anthu anazizwa ndi chiphunzitso chake: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo panakhala pamene Yesu anatha mau amenewa, makamu a anthu anazizwa ndi chiphunzitso chake: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Yesu atatsiriza kunena zimenezi, anthu onse aja adadabwa ndi kaphunzitsidwe kake, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Yesu atamaliza kunena zonsezi, magulu a anthu anadabwa ndi chiphunzitso chake, Onani mutuwo |