Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 7:27 - Buku Lopatulika

27 ndipo inagwa mvula, nidzala mitsinje, ndipo zinaomba mphepo, zinagunda pa nyumbayo; ndipo inagwa; ndi kugwa kwake kunali kwakukulu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 ndipo inagwa mvula, nidzala mitsinje, ndipo zinaomba mphepo, zinagunda pa nyumbayo; ndipo inagwa; ndi kugwa kwake kunali kwakukulu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Kudagwa mvula, mitsinje idadzaza, ndipo chimphepo chidadza nkuwomba pa nyumbayo, ndipo idagwa. Kugwa kwake kunali koopsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Mvula inagwa, mitsinje inadzaza, ndi mphepo zinawomba pa nyumbayo, ndipo inagwa ndipo kugwa kwake kunali kwakukulu.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 7:27
11 Mawu Ofanana  

Amene anakwatulidwa isanafike nyengo yao, chigumula chinakokolola kuzika kwao;


amene ndiwasungira tsiku la nsautso, tsiku lakulimbana nkhondo?


ndipo inagwa mvula, nidzala mitsinje, ndipo zinaomba mphepo, zinagunda pa nyumbayo; koma siinagwe; chifukwa inakhazikika pathanthwepo.


Ndipo yense akamva mau anga amenewa, ndi kusawachita, adzafanizidwa ndi munthu wopusa, yemwe anamanga nyumba yake pamchenga;


Ndipo panakhala pamene Yesu anatha mau amenewa, makamu a anthu anazizwa ndi chiphunzitso chake:


ntchito ya yense idzaonetsedwa; pakuti tsikulo lidzaisonyeza, chifukwa kuti yavumbululuka m'moto; ndipo moto wokha udzayesera ntchito ya yense ikhala yotani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa