Mateyu 7:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo yense akamva mau anga amenewa, ndi kusawachita, adzafanizidwa ndi munthu wopusa, yemwe anamanga nyumba yake pamchenga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo yense akamva mau anga amenewa, ndi kusawachita, adzafanizidwa ndi munthu wopusa, yemwe anamanga nyumba yake pamchenga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Koma aliyense wongomva mau angaŵa, osaŵagwiritsa ntchito, ali ngati munthu wopusa amene adaamanga nyumba yake pa mchenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Koma aliyense amene amva mawu angawa ndi kusawachita ali ngati munthu wopusa amene anamanga nyumba yake pa mchenga. Onani mutuwo |