Mateyu 7:29 - Buku Lopatulika29 pakuti anawaphunzitsa monga mwini mphamvu, wosanga alembi ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 pakuti anawaphunzitsa monga mwini mphamvu, wosanga alembi ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 chifukwa ankaŵaphunzitsa monga munthu waulamuliro osati monga m'mene ankachitira aphunzitsi a Malamulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 chifukwa anaphunzitsa ngati amene anali ndi ulamuliro osati ngati aphunzitsi amalamulo. Onani mutuwo |