Mateyu 26:2 - Buku Lopatulika2 Mudziwa kuti akapita masiku awiri, Paska afika, ndipo Mwana wa Munthu adzaperekedwa kupachikidwa pamtanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mudziwa kuti akapita masiku awiri, Paska afika, ndipo Mwana wa Munthu adzaperekedwa kupachikidwa pamtanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Pajatu chikondwerero cha Paska chiyambika patangopita masiku aŵiri, ndipo Mwana wa Munthu adzaperekedwa kuti akapachikidwe pa mtanda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Monga mukudziwa, kwatsala masiku awiri kuti Paska ifike ndipo Mwana wa Munthu adzaperekedwa kuti apachikidwe.” Onani mutuwo |