Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 22:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu anayankha, nalankhulanso kwa iwo m'mafanizo, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu anayankha, nalankhulanso kwa iwo m'mafanizo, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adalankhulanso ndi anthu aja m'mafanizo. Adati,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anayankhula nawonso mʼmafanizo, nati,

Onani mutuwo



Mateyu 22:1
9 Mawu Ofanana  

Ufumu wa Kumwamba ufanafana ndi munthu, mfumu, amene anakonzera mwana wake phwando la ukwati,


Koma anati kwa iye, Munthu wina anakonza phwando lalikulu; naitana anthu ambiri;


Ndipo Iye anati, Kwapatsidwa kwa inu kuzindikira zinsinsi za Ufumu wa Mulungu; koma kwa ena otsala ndinena nao mwa mafanizo; kuti pakuona sangaone, ndi pakumva sangadziwitse.