Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 22:2 - Buku Lopatulika

2 Ufumu wa Kumwamba ufanafana ndi munthu, mfumu, amene anakonzera mwana wake phwando la ukwati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ufumu wa Kumwamba ufanafana ndi munthu, mfumu, amene anakonzera mwana wake phwando la ukwati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 “Za Ufumu wakumwamba tingazifanizire motere: Mfumu ina idaakonzera mwana wake phwando laukwati.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Ufumu wakumwamba uli ngati mfumu imene inakonzera phwando mwana wake wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 22:2
15 Mawu Ofanana  

Fanizo lina Iye anawafotokozera iwo, nanena, Ufumu wa Kumwamba ufanizidwa ndi munthu, amene anafesa mbeu zabwino m'munda mwake;


Ndipo Yesu anayankha, nalankhulanso kwa iwo m'mafanizo, nati,


ndipo inu nokha khalani ofanana ndi anthu oyembekezera mbuye wao, pamene ati abwera kuchokera kuukwati; kuti pakudza iye, nakagogoda, akamtsegulire pomwepo.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Pakuti ndichita nsanje pa inu ndi nsanje ya Mulungu; pakuti ndinakupalitsani ubwenzi mwamuna mmodzi, kuti ndikalangize inu ngati namwali woyera mtima kwa Khristu.


Ndipo muchite monga momwe ananena mau akufotokozeraniwo, ku malo amene Yehova adzawasankha; nimusamalire kuchita monga mwa zonse akulangizanizi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa