Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 14:16 - Buku Lopatulika

16 Koma anati kwa iye, Munthu wina anakonza phwando lalikulu; naitana anthu ambiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Koma anati kwa iye, Munthu wina anakonza phwando lalikulu; naitana anthu ambiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Koma Yesu adamuphera fanizo, adati, “Munthu wina adaakonza phwando lalikulu, naitana anthu ambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Yesu anayankha kuti, “Munthu wina ankakonza phwando lalikulu ndipo anayitana alendo ambiri.

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:16
11 Mawu Ofanana  

Ndalowa m'munda mwanga, mlongo wanga, mkwatibwi: Ndatchera mure wanga ndi zonunkhiritsa zanga; ndadya uchi wanga ndi chisa chake; ndamwa vinyo wanga ndi mkaka wanga. Idyani, atsamwalinu, imwani, mwetsani chikondi.


Ndipo iwo a ku Efuremu adzakhala ngati ngwazi, ndi mtima wao udzakondwera ngati ndi vinyo; ndipo ana ao adzachiona nadzakondwera; mtima wao udzakondwerera mwa Yehova.


Ndipo Mzimu ndi mkwatibwi anena, Idzani. Ndipo wakumva anene, Idzani. Ndipo wakumva ludzu adze; iye wofuna, atenge madzi a moyo kwaulere.


Taona, ndaima pakhomo, ndigogoda; wina akamva mau anga nakatsegula pakhomo, ndidzalowa kwa iye, ndipo ndidzadya naye, ndi iye ndi Ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa