Luka 14:16 - Buku Lopatulika16 Koma anati kwa iye, Munthu wina anakonza phwando lalikulu; naitana anthu ambiri; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma anati kwa iye, Munthu wina anakonza phwando lalikulu; naitana anthu ambiri; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma Yesu adamuphera fanizo, adati, “Munthu wina adaakonza phwando lalikulu, naitana anthu ambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yesu anayankha kuti, “Munthu wina ankakonza phwando lalikulu ndipo anayitana alendo ambiri. Onani mutuwo |