Luka 14:17 - Buku Lopatulika17 ndipo anatumiza kapolo wake pa nthawi ya phwando kukanena kwa oitanidwawo, Idzani, chifukwa zonse zakonzeka tsopano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 ndipo anatumiza kapolo wake pa nthawi ya phwando kukanena kwa oitanidwawo, Idzani, chifukwa zonse zakonzeka tsopano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Nthaŵi ya phwando itakwana adatuma wantchito wake kukauza oitanidwa aja kuti, ‘Bwerani, pakuti zonse zakonzeka.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Nthawi yaphwando itakwana anatuma wantchito wake kuti akawuze onse amene anayitanidwa kuti, ‘Bwerani, pakuti zonse zakonzeka.’ Onani mutuwo |