Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 2:10 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo poona nyenyeziyo, anakondwera ndi kukondwera kwakukulu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo poona nyenyeziyo, anakondwera ndi kukondwera kwakukulu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ataiwona nyenyeziyo, adasangalala kwabasi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene iwo anaona nyenyeziyo, anasangalala kwambiri.

Onani mutuwo



Mateyu 2:10
9 Mawu Ofanana  

Mudzitamandire ndi dzina lake loyera: mitima yao ya iwo ofunsira Yehova ikondwere.


Anthu akondwere, nafuule mokondwera; pakuti mudzaweruza anthu molunjika, ndipo mudzalangiza anthu padziko lapansi.


Ndipo pofika kunyumba anaona kamwanako ndi Maria amake, ndipo anagwa pansi namgwadira Iye; namasula chuma chao, nampatsa Iye mitulo, ndiyo golide ndi lubani ndi mure.


Ndipo iwo, m'mene anamva mfumu, anamuka; ndipo onani, nyenyezi ija anaiona kum'mawa, inawatsogolera iwo, kufikira inadza nkuima pamwamba pomwe panali kamwanako.


Ndipo mngelo anati kwa iwo, Musaope; pakuti onani, ndikuuzani inu uthenga wabwino wa chikondwero chachikulu, chimene chidzakhala kwa anthu onse;


Ndipo abusawo anabwera, nalemekeza ndi kutamanda Mulungu pa zinthu zonse anazimva, naziona, monga kunalankhulidwa kwa iwo.


Anamuyendetsa pa misanje ya dziko lapansi, ndipo anadya zipatso za m'minda; namyamwitsa uchi wa m'thanthwe, ndi mafuta m'mwala wansangalabwe;