Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 2:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo iwo, m'mene anamva mfumu, anamuka; ndipo onani, nyenyezi ija anaiona kum'mawa, inawatsogolera iwo, kufikira inadza nkuima pamwamba pomwe panali kamwanako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo iwo, m'mene anamva mfumu, anamuka; ndipo onani, nyenyezi ija anaiona kum'mawa, inawatsogolera iwo, kufikira inadza niima pamwamba pomwe panali kamwanako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Anthu aja atamva mau a mfumu, adanyamuka. Nyenyezi imene adaaiwona kuvuma ija idaŵatsogolera mpaka idakafika nkukaima pamwamba pa malo amene panali mwanayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Atamva mawu a mfumu, ananyamuka ulendo wawo, ndipo taonani nyenyezi anayiona kummawa ija, inawatsogolera mpaka inayima pamwamba pa nyumba yomwe munali mwanayo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 2:9
7 Mawu Ofanana  

Munthuyo wakuopa Yehova ndani? Adzamlangiza iye njira adzasankheyo.


Akundikonda ndiwakonda; akundifunafuna adzandipeza.


Ndipo iwo poona nyenyeziyo, anakondwera ndi kukondwera kwakukulu.


nati, Ali kuti amene anabadwa mfumu ya Ayuda? Chifukwa tinaona nyenyezi yake kum'mawa, ndipo tinadzera kudzamlambira Iye.


Nawatumiza ku Betelehemu, nati, Yendani mufunitsitse za kamwanako; ndipo pamene mudzampeza, mundibwezere mau, kuti inenso ndidzadze kudzamlambira Iye.


Ndipo tili nao mau a chinenero okhazikika koposa; amene muchita bwino powasamalira, monga nyali younikira m'malo a mdima, kufikira kukacha, nikauka nthanda pa mtima yanu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa