Masalimo 105:3 - Buku Lopatulika3 Mudzitamandire ndi dzina lake loyera: mitima yao ya iwo ofunsira Yehova ikondwere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mudzitamandire ndi dzina lake loyera: mitima yao ya iwo ofunsira Yehova ikondwere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Munyadire dzina lake loyera. Ikondwe mitima ya anthu amene amapembedza Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Munyadire dzina lake loyera; mitima ya iwo amene amafunafuna Yehova ikondwere. Onani mutuwo |