Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 18:1 - Buku Lopatulika

Nthawi yomweyo ophunzira anadza kwa Yesu, nanena, Ndani kodi ali wopambana mu Ufumu wa Kumwamba?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nthawi yomweyo ophunzira anadza kwa Yesu, nanena, Ndani kodi ali wopambana mu Ufumu wa Kumwamba?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵi yomweyo ophunzira aja adadzamufunsa Yesu kuti, “Kodi mu Ufumu wakumwamba wamkulu koposa onse ndani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa nthawi imeneyo ophunzira anabwera kwa Yesu ndipo anamufunsa kuti, “Wamkulu woposa onse ndani mu ufumu wakumwamba?”

Onani mutuwo



Mateyu 18:1
13 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Yesu anaitana kamwana, anakaimitsa pakati pao,


Koma wamkulu wopambana wa inu adzakhala mtumiki wanu.


nanena, Tembenukani mitima; chifukwa Ufumu wa Kumwamba wayandikira.


Si yense wakunena kwa Ine, Ambuye, Ambuye, adzalowa mu Ufumu wa Kumwamba; koma wakuchitayo chifuniro cha Atate wanga wa Kumwamba.


M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;


musachite kanthu monga mwa chotetana, kapena monga mwa ulemerero wopanda pake, komatu ndi kudzichepetsa mtima, yense ayese anzake omposa iye mwini;