Mateyu 3:2 - Buku Lopatulika2 nanena, Tembenukani mitima; chifukwa Ufumu wa Kumwamba wayandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 nanena, Tembenukani mitima; chifukwa Ufumu wa Kumwamba wayandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ankati, “Tembenukani mtima chifukwa Mulungu ali pafupi kukhazikitsa ufumu wake tsopano.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 kuti, “Tembenukani mtima chifukwa ufumu wakumwamba wayandikira.” Onani mutuwo |