Mateyu 3:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti uyu ndiye ananenayo Yesaya mneneri, kuti, Mau a wofuula m'chipululu, konzani khwalala la Ambuye, lungamitsani njira zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti uyu ndiye ananenayo Yesaya mneneri, kuti, Mau a wofuula m'chipululu, konzani khwalala la Ambuye, lungamitsani njira zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Paja Yesaya ankanena za iyeyu pamene adaati, “Liwu la munthu wofuula m'chipululu: akunena kuti, ‘Konzani mseu wodzadzeramo Ambuye, ongolani njira zoti adzapitemo.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Uyu ndi amene mneneri Yesaya ananena za iye kuti, “Mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Konzani njira ya Ambuye, wongolani njira zake.’ ” Onani mutuwo |