Mateyu 23:11 - Buku Lopatulika11 Koma wamkulu wopambana wa inu adzakhala mtumiki wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma wamkulu wopambana wa inu adzakhala mtumiki wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pakati panupa wamkulu akhale mtumiki wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Wamkulu pakati panu adzakhala wokutumikirani. Onani mutuwo |