Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 23:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo musatchedwa atsogoleri, pakuti alipo mmodzi Mtsogoleri wanu, ndiye Khristu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo musatchedwa atsogoleri, pakuti alipo mmodzi Mtsogoleri wanu, ndiye Khristu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Anthu asatinso azikutchulani atsogoleri, popeza kuti Mtsogoleri wanu ndi mmodzi yekha, ndiye Khristu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Komanso musamatchedwenso ‘Mtsogoleri,’ pakuti muli naye Mtsogoleri mmodzi amene ndi Khristu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 23:10
5 Mawu Ofanana  

Koma wamkulu wopambana wa inu adzakhala mtumiki wanu.


Koma inu musatchedwa Rabi; pakuti Mphunzitsi wanu ali mmodzi, ndipo inu nonse muli abale.


Ndipo inu musatchule wina atate wanu pansi pano, pakuti alipo mmodzi ndiye Atate wanu wa Kumwamba.


Nati Iye, Mukani kumzinda kwa munthu wina wake, mukati kwa Iye, Mphunzitsi anena, Nthawi yanga yayandikira; ndidzadya Paska kwanu pamodzi ndi ophunzira anga.


Ndipo pali mautumiki osiyana, koma Ambuye yemweyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa