Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 17:8 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo, pokweza maso ao sanaone munthu, koma Yesu yekha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo, pokweza maso ao sanaone munthu, koma Yesu yekha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo aja poŵeramuka, adangoona kuti palibe munthu winanso, koma Yesu yekha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atayangʼana, sanaone wina aliyense kupatula Yesu yekha.

Onani mutuwo



Mateyu 17:8
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anadza, nawakhudza nati, Ukani, musaopa.


Ndipo pamene anali kutsika paphiri, Yesu anawalamula iwo kuti, Musakauze munthu choonekacho, kufikira Mwana wa Munthu adadzauka kwa akufa.


Ndipo dzidzidzi pounguzaunguza, sanapenye munthu wina yense, koma Yesu yekha, ndi iwo eni.


Ndipo pakutero mauwo, Yesu anapezedwa ali yekha. Ndipo iwo anakhala chete, ndipo sanauze munthu aliyense masiku aja kanthu konse ka izo anaziona.