Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 9:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo pakutero mauwo, Yesu anapezedwa ali yekha. Ndipo iwo anakhala chete, ndipo sanauze munthu aliyense masiku aja kanthu konse ka izo anaziona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo pakutero mauwo, Yesu anapezedwa ali yekha. Ndipo iwo anakhala chete, ndipo sanauze munthu aliyense masiku aja kanthu konse ka izo anaziona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Mauwo atamveka choncho, ophunzira aja adaona kuti Yesu ali yekha. Iwo adangokhala chete masiku amenewo, osauza wina aliyense zimene adaaziwonazo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Atamveka mawuwa, anaona kuti Yesu anali yekha. Ophunzirawo anazisunga izi mwa iwo okha ndipo sanawuze wina aliyense pa nthawiyi za zomwe iwo anaziona.

Onani mutuwo Koperani




Luka 9:36
4 Mawu Ofanana  

mphindi yakung'amba ndi mphindi yakusoka; mphindi yakutonthola ndi mphindi yakulankhula;


Ndipo pamene anali kutsika paphiri, Yesu anawalamula iwo kuti, Musakauze munthu choonekacho, kufikira Mwana wa Munthu adadzauka kwa akufa.


Pakuti sanadziwe chimene adzayankha; chifukwa anachita mantha ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa