Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 15:7 - Buku Lopatulika

Onyenga inu! Yesaya ananenera bwino za inu, ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Onyenga inu! Yesaya ananenera bwino za inu, ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu anthu achiphamaso, ndithu mneneri Yesaya adaanenadi zoona muja adaati,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu anthu achiphamaso, Yesaya ananenera za inu kuti,

Onani mutuwo



Mateyu 15:7
7 Mawu Ofanana  

ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati nkhanambo yapitirira khungu, wansembe amutche wodetsedwa, ndilo khate.


iyeyo sadzalemekeza atate wake. Ndipo inu mupeputsa mau a Mulungu chifukwa cha miyambo yanu.


Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao; koma mtima wao uli kutali ndi Ine.


Wonyenga iwe! Tayamba kuchotsa m'diso lako mtandawo, ndipo pomwepo udzapenyetsa kuchotsa kachitsotso m'diso la mbale wako.


Ndipo Iye ananena nao, Yesaya ananenera bwino za inu onyenga, monga mwalembedwa, Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao, koma mtima wao ukhala kutali ndi Ine.