Mateyu 15:8 - Buku Lopatulika8 Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao; koma mtima wao uli kutali ndi Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao; koma mtima wao uli kutali ndi Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “ ‘Anthu aŵa amangondilemekeza ndi pakamwa chabe, koma mtima wao uli kutali ndi Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “ ‘Anthu awa amandilemekeza Ine ndi milomo yawo, koma mitima yawo ili kutali ndi Ine. Onani mutuwo |