Mateyu 15:9 - Buku Lopatulika9 Koma andilambira Ine kwachabe, ndi kuphunzitsa maphunzitso, malangizo a anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma andilambira Ine kwachabe, ndi kuphunzitsa maphunzitso, malangizo a anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Amandipembedza inde, koma kupembedza kwaoko nkopanda phindu, chifukwa zimene amaphunzitsa ngati zophunzitsa zenizeni ndi malamulo a anthu chabe.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Amandilambira Ine kwachabe ndi kuphunzitsa malamulo ndi malangizo a anthu.’ ” Onani mutuwo |