Levitiko 13:8 - Buku Lopatulika8 ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati nkhanambo yapitirira khungu, wansembe amutche wodetsedwa, ndilo khate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati nkhanambo yapitirira khungu, wansembe amutche wodetsedwa, ndilo khate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Wansembe amuwonetsetsenso munthuyo. Akaona kuti m'bukowo wafalikiradi pa khungu, atchule wodwalayo kuti ndi woipitsidwa, limenelo ndi khate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Wansembe amuonetsetsenso munthuyo, ndipo ngati mʼbukowo wafalikira pa khungu, wansembe alengeze kuti munthuyo ndi wodetsedwa ndi kuti nthendayo ndi khate. Onani mutuwo |