Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 13:9 - Buku Lopatulika

9 Pamene nthenda yakhate ili mwa munthu, azimfikitsa kwa wansembe;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Pamene nthenda yakhate ili mwa munthu, azimfikitsa kwa wansembe;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 “Munthu akagwidwa ndi nthenda ya khate, abwere naye kwa wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 “Ngati munthu aliyense ali ndi nthenda ya pakhungu yoyipitsa thupi, wodwalayo abwere naye kwa wansembe.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:9
3 Mawu Ofanana  

ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati pali chotupa choyera pakhungu, ndipo chasanduliza tsitsi likhale loyera, ndipo pachotupa pali mnofu wofiira,


Ngati munthu ali nacho chotupa, kapena nkhanambo, kapena chikanga pa khungu la thupi lake, ndipo isandulika nthenda yakhate pa khungu la thupi lake, azifika kwa Aroni wansembe, kapena kwa mmodzi wa ana ake ansembe;


ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati nkhanambo yapitirira khungu, wansembe amutche wodetsedwa, ndilo khate.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa