Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:10 - Buku Lopatulika

10 ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati pali chotupa choyera pakhungu, ndipo chasanduliza tsitsi likhale loyera, ndipo pachotupa pali mnofu wofiira,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati pali chotupa choyera pakhungu, ndipo chasanduliza tsitsi likhale loyera, ndipo pachotupa pali mnofu wofiira,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Wansembe amuwonetsetse. Akakhala ndi chithupsa cha maonekedwe oyera pa khungu, chimene chasandutsa ubweya wapamalopo kukhala woyera, ndipo pachithupsapo pakakhala zilonda,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Wansembe amuonetsetse munthuyo, ndipo ngati ali ndi chithupsa chamaonekedwe woyera pa khungupo chimene chasandutsa ubweya wa pamalopo kukhala woyera, ndipo ngati pali zilonda pa chotupacho,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:10
12 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake khate la Naamani lidzakumamatira iwe ndi mbumba yako chikhalire. Ndipo anatuluka pamaso pake wakhate wa mbuu ngati chipale chofewa.


Wokonda mwambo akonda kudziwa; koma wakuda chidzudzulo apulukira.


ndilo khate lakale pa khungu la thupi lake, ndipo wansembe amutche wodetsedwa; asambindikiretse popeza ali wodetsedwa.


Kapena pamene thupi lidapsa ndi moto pakhungu pake, ndipo mnofu wofiira wakupsawo usanduka chikanga chotuuluka, kapena chotuwa;


Pamene nthenda yakhate ili mwa munthu, azimfikitsa kwa wansembe;


Iwo adana naye wodzudzula kuchipata, nanyansidwa naye wolunjikitsa mau.


Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa