Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 15:6 - Buku Lopatulika

6 iyeyo sadzalemekeza atate wake. Ndipo inu mupeputsa mau a Mulungu chifukwa cha miyambo yanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 iyeyo sadzalemekeza atate wake. Ndipo inu mupeputsa mau a Mulungu chifukwa cha miyambo yanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Pakutero, chifukwa cha mwambo wanuwo, mau a Mulungu inu mumaŵasandutsa achabechabe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 iye sakulemekeza nayo abambo ake ndipo ndi khalidwe lotere inu mumapeputsa nalo Mawu a Mulungu chifukwa cha mwambo wanu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:6
12 Mawu Ofanana  

Yafika nyengo yakuti Yehova achite kanthu; pakuti anaswa chilamulo chanu.


Changu changa chinandithera, popeza akundisautsa anaiwala mau anu.


Bwanji muti, Tili ndi nzeru ife, ndi malamulo a Yehova ali ndi ife? Koma, taona, peni lonyenga la alembi lachita zonyenga.


Anthu anga aonongeka chifukwa cha kusadziwa; popeza unakana kudziwa, Inenso ndikukaniza, kuti usakhale wansembe wanga; popeza waiwala chilamulo cha Mulungu wako, Inenso ndidzaiwala ana ako.


Koma inu munena, Aliyense amene anena kwa atate wake kapena kwa amake, Icho ukanathandizidwa nacho, nchoperekedwa kwa Mulungu;


Onyenga inu! Yesaya ananenera bwino za inu, ndi kuti,


muyesa achabe mau a Mulungu mwa mwambo wanu, umene munaupereka: ndi zinthu zotere zambiri muzichita.


Potero kodi lamulo tiyesa chabe mwa chikhulupiriro? Msatero ai; koma tikhazikitsa lamulo.


Ngati mkazi wina wokhulupirira ali nao amasiye, iye awathandize, ndipo Mpingowo usalemedwe; kuti uthandize iwo amene ali amasiye ndithu.


Koma ngati wina sadzisungiratu mbumba yake ya iye yekha, makamaka iwo a m'banja lake, wakana chikhulupiriro iye, ndipo aipa koposa wosakhulupirira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa