Mateyu 15:6 - Buku Lopatulika6 iyeyo sadzalemekeza atate wake. Ndipo inu mupeputsa mau a Mulungu chifukwa cha miyambo yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 iyeyo sadzalemekeza atate wake. Ndipo inu mupeputsa mau a Mulungu chifukwa cha miyambo yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pakutero, chifukwa cha mwambo wanuwo, mau a Mulungu inu mumaŵasandutsa achabechabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 iye sakulemekeza nayo abambo ake ndipo ndi khalidwe lotere inu mumapeputsa nalo Mawu a Mulungu chifukwa cha mwambo wanu. Onani mutuwo |