Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 8:9 - Buku Lopatulika

Yehova, Ambuye wathu, dzina lanu liposadi nanga padziko lonse lapansi!

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova, Ambuye wathu, dzina lanu liposadi nanga pa dziko lonse lapansi!

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta, Ambuye athu, dzina lanu ndi lotchuka pa dziko lonse lapansi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!

Onani mutuwo



Masalimo 8:9
4 Mawu Ofanana  

Kodi ukhoza kupeza Mulungu mwa mufunafuna? Ukhoza kupeza Wamphamvuyonse motsindika?


Ntchito zanu zichulukadi, Yehova! Munazichita zonse mwanzeru; dziko lapansi lidzala nacho chuma chanu.


Yehova, Ambuye wathu, dzina lanu liposadi nanga padziko lonse lapansi! Inu amene munaika ulemerero wanu pa thambo la kumwamba.


Palibe wina ngati Mulungu, Yesuruni iwe, wakuyenda wokwera pathambo, kukuthandiza, ndi pa mitambo mu ukulu wake.