Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 51:9 - Buku Lopatulika

Muzibisire nkhope yanu zolakwa zanga, ndipo mufafanize mphulupulu zanga zonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Muzibisire nkhope yanu zolakwa zanga, ndipo mufafanize mphulupulu zanga zonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mufulatire machimo anga, mufafanize zoipa zanga zonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mufulatire machimo anga ndi kufafaniza zolakwa zanga zonse.

Onani mutuwo



Masalimo 51:9
9 Mawu Ofanana  

Ndikasamba madzi a chipale chofewa ndi kuyeretsa manja anga ndi sopo.


Mundichitire ine chifundo, Mulungu, monga mwa kukoma mtima kwanu; monga mwa unyinji wa nsoni zanu zokoma mufafanize machimo anga.


Tiyeni, tsono, tiweruzane, ati Yehova; ngakhale zoipa zanu zili zofiira, zidzayera ngati matalala; ngakhale zili zofiira ngati kapezi, zidzakhala ngati ubweya wa nkhosa, woti mbuu.


Taonani, ndinali ndi zowawa zazikulu, chifukwa cha mtendere wanga; Koma Inu mokonda moyo wanga, munaupulumutsa m'dzanja la chivundi, Pakuti mwaponya m'mbuyo mwanu machimo anga onse.


Pakuti maso anga ali panjira zao zonse, sabisika pa nkhope yanga, mphulupulu yao siibisika pamaso panga.


Ndipo ndidzakuwazani madzi oyera, ndipo mudzakhala oyera; ndidzakuyeretsani kukuchotserani zodetsa zanu zonse, ndi mafano anu nonse.


ndi munthu woyera atenge hisope, namviike m'madzimo, ndi kuwawaza pahema ndi pa zotengera zonse, ndi pa anthu anali pomwepo, ndi pa iye wakukhudza fupa, kapena wophedwa, kapena wakufa, kapena manda.


adatha kutifafanizira cha pa ifecho cholembedwa m'zoikikazo, chimene chinali chotsutsana nafe: ndipo anachichotsera pakatipo, ndi kuchikhomera ichi pamtanda;