Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 24:9 - Buku Lopatulika

Weramutsani mitu yanu, zipata inu; inde weramutsani, zitseko zosatha inu, kuti Mfumu ya ulemerero ilowe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Weramutsani mitu yanu, zipata inu; inde weramutsani, zitseko zosatha inu, kuti Mfumu ya ulemerero ilowe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kankhani zipata za mzinda, tsekulani zitseko zakalekalezo, kuti Mfumu yaulemerero iloŵe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tukulani mitu yanu, inu zipata; tsekukani, inu zitseko zakalekalenu, kuti Mfumu yaulemerero ilowe.

Onani mutuwo



Masalimo 24:9
1 Mawu Ofanana  

Chipata cha Yehova ndi ichi; olungama adzalowamo.