Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 22:4 - Buku Lopatulika

Makolo athu anakhulupirira Inu; anakhulupirira, ndipo munawalanditsa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Makolo athu anakhulupirira Inu; anakhulupirira, ndipo munawalanditsa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Makolo athu ankadalira Inu. Zoonadi, ankakhulupirira Inu, ndipo Inu munkaŵapulumutsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa inu makolo athu anadalira; iwo anadalira ndipo Inu munawapulumutsa.

Onani mutuwo



Masalimo 22:4
10 Mawu Ofanana  

Ndipo anakhulupirira Yehova, ndipo kunayesedwa kwa iye chilungamo.


Ndipo anati, Dzina lako silidzatchedwanso Yakobo, koma Israele, chifukwa unayesana naye Mulungu ndithu, ndipo unapambana.


Ndipo kunali, pakuchita limodzi amalipenga ndi oimba, kumveketsa mau amodzi akulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi pakukweza mau ao pamodzi ndi malipenga, ndi nsanje, ndi zoimbira zina, ndi kulemekeza Yehova, ndi kuti, Pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake chikhala chikhalire; pamenepo mtambo unadzaza nyumbayi, ndiyo nyumba ya Yehova;


Ndipo Israele anaiona ntchito yaikulu imene Yehova anachitira Aejipito, ndipo anthuwo anaopa Yehova; nakhulupirira Yehova ndi mtumiki wake Mose.