Masalimo 22:5 - Buku Lopatulika5 Anafuula kwa Inu, napulumutsidwa; anakhulupirira Inu, ndipo sanachite manyazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Anafuula kwa Inu, napulumutsidwa; anakhulupirira Inu, ndipo sanachite manyazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ankalirira Inu, ndipo Inu munkaŵalanditsa. Ankakhulupirira Inu, ndipo Inu simunkaŵagwiritsa mwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Analirira kwa inu ndipo munawapulumutsa. Iwo anakhulupirira Inu ndipo simunawakhumudwitse. Onani mutuwo |