Masalimo 22:6 - Buku Lopatulika6 Koma ine ndine nyongolotsi, si munthu ai, chotonza cha anthu, ndi wonyozedwa ndi anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma ine ndine nyongolotsi, si munthu ai, chotonza cha anthu, ndi wonyozedwa ndi anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma ine ndine nyongolotsi, sindine munthu konse, ndine amene anthu onse amandinyodola ndi kundinyoza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma ine ndine nyongolotsi osati munthu, wosekedwa ndi wonyozedwa ndi anthu onse. Onani mutuwo |