Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 148:7 - Buku Lopatulika

Lemekezani Yehova kochokera ku dziko lapansi, zinsomba inu, ndi malo ozama onse;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Lemekezani Yehova kochokera ku dziko lapansi, zinsomba inu, ndi malo ozama onse;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tamandani Chauta inu okhala pa dziko lapansi, inu zilombo za m'madzi ndi nyanja zonse zozama,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tamandani Yehova pa dziko lapansi, inu zolengedwa zikuluzikulu za mʼnyanja, ndi nyanja zonse zakuya,

Onani mutuwo



Masalimo 148:7
9 Mawu Ofanana  

Mulungu ndipo adalenga zinsomba zazikulu ndi zoyendayenda zamoyo zakuchuluka m'madzi mwa mitundu yao, ndi mbalame zamapiko, yonse monga mwa mtundu wake: ndipo anaona Mulungu kuti kunali kwabwino.


Namuka iye, napeza mtembo wake wogwera m'njira, ndi bulu ndi mkango zili chiimire pafupi ndi mtembo. Mkango udalibe kudya mtembo, kapena kukadzula bulu.


Ntchito zanu zichulukadi, Yehova! Munazichita zonse mwanzeru; dziko lapansi lidzala nacho chuma chanu.


Tsiku limenelo Yehova ndi lupanga lake lolimba ndi lalikulu ndi lamphamvu adzalanga Leviyatani njoka yothamanga, ndi Leviyatani njoka yopindikapindika; nadzapha ching'ona chimene chili m'nyanja.


Nyama za m'thengo zidzandilimekeza, ankhandwe ndi nthiwatiwa; chifukwa ndipatsa madzi m'chipululu, ndi mitsinje m'mkhwangwala, ndimwetse anthu anga osankhika;