Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:2 - Buku Lopatulika

Anene tsono Israele, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anene tsono Israele, kuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Aisraele anene kuti, “Chikondi chake nchamuyaya.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Israeli anene kuti: “Chikondi chake ndi chosatha.”

Onani mutuwo



Masalimo 118:2
7 Mawu Ofanana  

Ntchito zanu zonse zidzakuyamikani, Yehova; ndi okondedwa anu adzakulemekezani.


Ndipo onse amene atsata chilangizo ichi, mtendere ndi chifundo zikhale pa iwo, ndi pa Israele wa Mulungu.


Potero mwa Iye tipereke chiperekere nsembe yakuyamika Mulungu, ndiyo chipatso cha milomo yovomereza dzina lake.