Masalimo 145:10 - Buku Lopatulika10 Ntchito zanu zonse zidzakuyamikani, Yehova; ndi okondedwa anu adzakulemekezani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ntchito zanu zonse zidzakuyamikani, Yehova; ndi okondedwa anu adzakulemekezani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Zamoyo zonse zidzakuthokozani, Inu Chauta, anthu anu onse oyera mtima adzakutamandani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Zonse zimene munazipanga zidzakutamandani, Inu Yehova; oyera mtima adzakulemekezani. Onani mutuwo |