Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 10:10 - Buku Lopatulika

Aunthama, nawerama, ndipo aumphawi agwa m'zala zake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Aunthama, nawerama, ndipo aumphawi agwa m'zala zake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amambwandira ndi kupsitiriza anthu osoŵa mwai, ndipo nyonga zake zimaŵagwetsa pansi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthuwo amawapondaponda ndipo amakomoka; amakhala pansi pa mphamvu zake.

Onani mutuwo



Masalimo 10:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo kunatero kuti pakusendera munthu aliyense kudzamlambira, iye anatambasula dzanja lake, namgwira, nampsompsona.


Ndipo kudzali kuti yense wakusiyidwa wa m'banja lako adzabwera kwa iye nadzawerama ndi kupempha ndalama ndi chakudya, nadzati, Mundipatsetu ntchito ina ya wansembe, kuti ndikaone kakudya.