Masalimo 10:9 - Buku Lopatulika9 Alalira monga mkango m'ngaka mwake; alalira kugwira wozunzika, agwira wozunzika, pakumkola mu ukonde mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Alalira monga mkango m'ngaka mwake; alalira kugwira wozunzika, agwira wozunzika, pakumkola m'ukonde mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Amabisalira osauka ngati mkango m'ngaka yake, amabisalira osauka kuti aŵagwire. Osaukawo amaŵagwiradi akaŵakokera mu ukonde wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Amabisalira anthu ngati mkango pa zitsamba. Amabisalira kuti agwire anthu opanda mphamvu; amagwira anthu opanda mphamvu ndi kuwakokera mu ukonde wake. Onani mutuwo |