Masalimo 10:8 - Buku Lopatulika8 Akhala m'molalira midzi; mobisalamo akupha munthu wosachimwa. Ambisira waumphawi nkhope yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Akhala m'molalira midzi; mobisalamo akupha munthu wosachimwa. Ambisira waumphawi nkhope yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Amalalira m'midzi, amapha anthu osalakwa m'malo obisalira. Amazondazonda kuti apeze opanda mwai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iye amabisalira anthu pafupi ndi midzi, kuchokera pobisalapo amapha anthu osalakwa, amayangʼanayangʼana mwachinsinsi anthu oti awawononge. Onani mutuwo |