Masalimo 10:7 - Buku Lopatulika7 M'kamwa mwake mwadzala kutemberera ndi manyengo ndi kuchenjerera; pansi pa lilime lake pali chivutitso chopanda pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 M'kamwa mwake mwadzala kutemberera ndi manyengo ndi kuchenjerera; pansi pa lilime lake pali chivutitso chopanda pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pakamwa pake pamangolankhula zotemberera, zonyenga ndi zoopseza. M'kamwa mwake mumatuluka zovutitsa ena ndiponso zoipa zokhazokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mʼkamwa mwake mwadzaza matemberero, mabodza ndi zoopseza; zovutitsa ndi zoyipa zili pansi pa lilime lake. Onani mutuwo |