Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 4:11 - Buku Lopatulika

Ndipo, Pa manja ao adzakunyamula iwe, kuti ungagunde konse phazi lako pamwala.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo, Pa manja ao adzakunyamula iwe, kuti ungagunde konse phazi lako pamwala.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“ ‘Iwo adzakunyamulani m'manja mwao, kuti mapazi anu angapweteke pa miyala.’ ”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo adzakunyamula ndi manja awo, kuti phazi lako lisagunde pa mwala.”

Onani mutuwo



Luka 4:11
3 Mawu Ofanana  

Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe, akusunge m'njira zako zonse.


Adzakunyamula pa manja ao, ungagunde phazi lako pamwala.


nanena naye, Ngati muli Mwana wa Mulungu, mudzigwetse nokha pansi: pakuti kwalembedwa, kuti, Adzalamula angelo ake za iwe, ndipo pa manja ao adzakunyamula iwe, ungagunde konse phazi lako pamwala.