Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 3:10 - Buku Lopatulika

Ndipo anthu a makamu anamfunsa iye, nanena, Ndipo tsono tizichita chiyani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anthu a makamu anamfunsa iye, nanena, Ndipo tsono tizichita chiyani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo anthu aja adafunsa Yohane kuti, “Tsono ife tizichita zabwino zanji?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Gulu la anthuwo linafunsa kuti, “Nanga tsono tichite chiyani?”

Onani mutuwo



Luka 3:10
7 Mawu Ofanana  

Ndipo amisonkho omwe anadza kudzabatizidwa, nati kwa iye, Mphunzitsi, ife tizichita chiyani?


Ndipo asilikali omwe anamfunsa iye, nati, Nanga ife tizichita chiyani? Ndipo iye anati kwa iwo, Musaopse, musanamize munthu aliyense; khalani okhuta ndi kulipira kwanu.


Chifukwa chake balani zipatso zakuyenera kulapa mtima, ndipo musayambe kunena mwa inu nokha, Atate wathu tili naye ndiye Abrahamu: pakuti ndinena kwa inu, kuti ali ndi mphamvu Mulungu, mwa miyala iyi, kuukitsira Abrahamu ana.


nawatulutsira iwo kunja, nati, Ambuye, ndichitenji kuti ndipulumuke?


Koma pamene anamva ichi, analaswa mtima, natitu kwa Petro ndi atumwi enawo, Tidzachita chiyani, amuna inu, abale?


Koma Petro anati kwa iwo, Lapani, batizidwani yense wa inu m'dzina la Yesu Khristu kuloza ku chikhululukiro cha machimo anu; ndipo mudzalandira mphatso ya Mzimu Woyera.


komatu, uka, nulowe m'mzinda, ndipo kudzanenedwa kwa iwe chimene uyenera kuchita.