Machitidwe a Atumwi 2:37 - Buku Lopatulika37 Koma pamene anamva ichi, analaswa mtima, natitu kwa Petro ndi atumwi enawo, Tidzachita chiyani, amuna inu, abale? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Koma pamene anamva ichi, analaswa mtima, natitu kwa Petro ndi atumwi enawo, Tidzachita chiyani, amuna inu, abale? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Pamene anthu aja anamva zimenezi, zidaŵalasa mtima, ndipo adafunsa Petro ndi atumwi ena aja kuti, “Abale, tsono ifeyo tichite chiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Anthu atamva zimenezi, anatsutsika kwambiri mu mtima ndipo anati kwa Petro ndi atumwi enawo, “Abale, kodi ife tichite chiyani?” Onani mutuwo |