Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:1 - Buku Lopatulika

Koma tsiku loyamba la sabata, mbandakucha, anadza kumanda atatenga zonunkhira adazikonza.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma tsiku loyamba la sabata, mbandakucha, anadza kumanda atatenga zonunkhira adazikonza.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'mamaŵa pa tsiku lotsatira Sabata ya Ayuda, azimai aja adapita ku manda, atatenga zonunkhira zimene adaakakonza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa tsiku loyamba la Sabata, mmamawa kwambiri, amayi anatenga zonunkhira napita ku manda.

Onani mutuwo



Luka 24:1
10 Mawu Ofanana  

Ndipo analinso kumeneko akazi akuyang'anira kutali; mwa iwo anali Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo wamng'ono ndi wa Yosefe, ndi Salome;


Koma panali Maria wa Magadala, ndi Yohana, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi akazi ena pamodzi nao amene ananena izi kwa atumwiwo.


Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda.


Komatu akazi enanso a mwa ife anatidabwitsa, ndiwo amene analawirira kumanda;