Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 11:3 - Buku Lopatulika

tipatseni ife tsiku ndi tsiku chakudya cha patsiku.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

tipatseni ife tsiku ndi tsiku chakudya cha patsiku.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mutipatse ife tsiku lililonse chakudya chathu chamasikuwonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mutipatse chakudya chathu chalero,

Onani mutuwo



Luka 11:3
7 Mawu Ofanana  

Mundichotsere kutali zachabe ndi mabodza; musandipatse umphawi, ngakhale chuma, mundidyetse zakudya zondiyenera;


iye adzakhala pamsanje; malo ake ochinjikiza adzakhala malinga amiyala; chakudya chake chidzapatsidwa kwa iye; madzi ake adzakhala chikhalire.


Mutipatse ife lero chakudya chathu chalero.


Chifukwa chake musadere nkhawa za mawa; pakuti mawa adzadzidera nkhawa iwo okha. Zikwanire tsiku zovuta zake.


Amenewa anali mfulu koposa a mu Tesalonika, popeza analandira mau ndi kufunitsa kwa mtima wonse, nasanthula m'malembo masiku onse, ngati zinthu zinali zotero.