Rubeni, ndiwe woyamba wanga, mphamvu yanga ndi chiyambi cha mphamvu yanga; ulemu wopambana, ndi mphamvu yopambana.
Genesis 49:2 - Buku Lopatulika Sonkhanani, tamvani, ana aamuna a Yakobo; tamverani Israele atate wanu. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Sonkhanani, tamvani, ana amuna a Yakobo; tamverani Israele atate wanu. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa “Bwerani kuno, ndipo mumve, inu ana a Yakobe, mverani bambo wanu Israele. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero “Bwerani ndipo imvani mawu anga, inu ana a Yakobo; mverani abambo anu Israeli. |
Rubeni, ndiwe woyamba wanga, mphamvu yanga ndi chiyambi cha mphamvu yanga; ulemu wopambana, ndi mphamvu yopambana.
Sonkhanani inu nonse ndi kumva, ndani mwa iwo aonetsa zinthu izi? Iye amene Yehova anamkonda, iye adzachita kufuna kwake pa Babiloni, ndi mkono wake udzakhala pa Ababiloni.