Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 34:11 - Buku Lopatulika

11 Idzani ananu ndimvereni ine, ndidzakulangizani zakumuopa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Idzani ananu ndimvereni ine, ndidzakulangizani zakumuopa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Bwerani ana anga, mundimvere, ndidzakuphunzitsani kuwopa Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Bwerani ana anga, mundimvere; ndidzakuphunzitsani kuopa Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 34:11
20 Mawu Ofanana  

Mkango wokalamba udzifera posowa mkoka, ndi misona ya mkango waukazi imwazika.


Pakuti akhutitsa mtima wolakalaka, nadzaza mtima wanjala ndi zabwino.


Kumuopa Yehova ndiko chiyambi cha nzeru; onse akuchita chotero ali nacho chidziwitso chokoma; chilemekezo chake chikhalitsa kosatha.


M'nyumba mwake mudzakhala akatundu ndi chuma: Ndi chilungamo chake chikhala chikhalire.


Yehova ndiye mbusa wanga; sindidzasowa.


Ine ndidzakulangiza ndi kuphunzitsa iwe za njira ukayendayo; ndidzakupangira ndi diso langa lakuyang'ana iwe.


Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu, ndipo ndidzafotokozera zonse anazichitira moyo wanga.


Kuopa Yehova ndiko chiyambi cha kudziwa; opusa anyoza nzeru ndi mwambo.


Phunzitsa mwana poyamba njira yake; ndipo angakhale atakalamba sadzachokamo.


Ananu, mverani mwambo wa atate, nimutchere makutu mukadziwe luntha;


Ndipo tsopano, ananga, mundimvere ine, labadirani mau a m'kamwa mwanga.


Akundikonda ndiwakonda; akundifunafuna adzandipeza.


Ndipo tsopano, ananga, mundimvere ine, ngodala akusunga njira zanga.


Kondwera ndi unyamata wako, mnyamata iwe; mtima wako nukasangalale masiku a unyamata wako, nuyende m'njira za mtima wako, ndi monga maso ako aona; koma dziwitsa kuti Mulungu adzanena nawe mlandu wa zonsezi.


Kodi Mulungu adzaphunzitsa yani nzeru? Kodi Iye adzamvetsa yani uthengawo? Iwo amene aletsedwa kuyamwa, nachotsedwa pamawere?


Tiana, katsala kanthawi ndikhala ndi inu. Mudzandifunafuna Ine; ndipo monga ndinanena kwa Ayuda, kuti kumene ndinkako Ine, inu simungathe kudza, momwemo ndinena kwa inu tsopano.


ndi kuti kuyambira ukhanda wako wadziwa malembo opatulika, okhoza kukupatsa nzeru kufikira chipulumutso, mwa chikhulupiriro cha mwa Khristu Yesu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa